Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:23 - Buku Lopatulika

23 ndipo m'mene sanapeze mtembo wake, anadza, nanena kuti adaona m'masomphenya angelo, amene ananena kuti ali ndi moyo Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 ndipo m'mene sanapeze mtembo wake, anadza, nanena kuti adaona m'masomphenya angelo, amene ananena kuti ali ndi moyo Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 ndiye amati sadaupeze mtembo wake. Tsono atabwerako amadzasimba kuti anaona angelo amene anaŵauza kuti Yesu ali moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 koma sanakapeze mtembo wake. Iwo anabwera ndi kudzatiwuza ife kuti anaona masomphenya a angelo amene anati Yesu ali moyo.

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:23
6 Mawu Ofanana  

Iye mulibe muno iai; pakuti anauka, monga ananena. Idzani muno mudzaone malo m'mene anagonamo Ambuye.


Ndipo iwowo, pamene anamva kuti ali moyo, ndi kuti adapenyeka kwa iye, sanamvere.


Komatu akazi enanso a mwa ife anatidabwitsa, ndiwo amene analawirira kumanda;


Ndipo ena a iwo anali nafe anachoka kunka kumanda, napeza monga momwe akazi adanena; koma Iyeyo sanamuone.


Ndipo m'mene analowa sanapeze mtembo wa Ambuye Yesu.


Maria wa Magadala anapita, nalalikira kwa ophunzirawo, kuti, Ndaona Ambuye; ndi kuti ananena izi kwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa