Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Luka 24:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo ena a iwo anali nafe anachoka kunka kumanda, napeza monga momwe akazi adanena; koma Iyeyo sanamuone.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo ena a iwo anali nafe anachoka kunka kumanda, napeza monga momwe akazi adanena; koma Iyeyo sanamuone.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Ena mwa ife anapita kumandako, ndipo anakapezadi monga momwe azimai aja amasimbira, koma Iyeyo sadamuwone ai.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Kenaka ena mwa anzathu anapita ku manda ndipo anakapeza monga momwe amayiwo ananenera, koma Iye sanamuone.”

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:24
5 Mawu Ofanana  

Pomwepo Herode anawaitana Anzeruwo m'tseri, nafunsitsa iwo nthawi yake idaoneka nyenyeziyo.


Koma Petro ananyamuka nathamangira kumanda, ndipo powerama anaona nsalu zabafuta pazokha; ndipo anachoka nanka kwao, nazizwa ndi chija chidachitikacho.


ndipo m'mene sanapeze mtembo wake, anadza, nanena kuti adaona m'masomphenya angelo, amene ananena kuti ali ndi moyo Iye.


Ndipo Iye anati kwa iwo, Opusa inu, ndi ozengereza mtima kusakhulupirira zonse adazilankhula aneneri!


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa