Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Luka 24:22 - Buku Lopatulika

22 Komatu akazi enanso a mwa ife anatidabwitsa, ndiwo amene analawirira kumanda;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Komatu akazi enanso a mwa ife anatidabwitsa, ndiwo amene analawirira kumanda;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Komanso azimai ena a m'gulu lathu anatidabwitsa. Iwowo anapita ku manda m'mamaŵa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Kuwonjezanso apo, ena mwa amayi athu atidabwitsa ife. Iwo anapita ku manda mmamawa

Onani mutuwo Koperani




Luka 24:22
6 Mawu Ofanana  

ndipo m'mene sanapeze mtembo wake, anadza, nanena kuti adaona m'masomphenya angelo, amene ananena kuti ali ndi moyo Iye.


Maria wa Magadala anapita, nalalikira kwa ophunzirawo, kuti, Ndaona Ambuye; ndi kuti ananena izi kwa iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa