Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Luka 10:8 - Buku Lopatulika

Ndipo m'mudzi uliwonse mukalowamo, ndipo alandira inu, idyani zomwezi akupatsani;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo m'mudzi uliwonse mukalowamo, ndipo alandira inu, idyani zomwezi akupatsani;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mukaloŵa m'mudzi, anthu nakulandirani, mudye zimene akukonzerani.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Mukamalowa mʼmudzi, ndi kulandiridwa, idyani chilichonse akukonzerani.

Onani mutuwo



Luka 10:8
6 Mawu Ofanana  

Iye wakulandira inu, andilandira Ine, ndi wakundilandira Ine, amlandira Iye amene ananditumiza Ine.


ndipo salandira inu, m'mene mwatuluka kumakwalala ake nenani,


Amene aliyense akalandire kamwana aka m'dzina langa alandira Ine; ndipo amene andilandira Ine alandira Iye amene anandituma Ine; pakuti iye wakukhala wamng'onong'ono wa inu nonse, yemweyu ndiye wamkulu.


Indetu, indetu, ndinena ndi inu, Iye wolandira aliyense amene ndimtuma, andilandira Ine; koma wolandira Ine alandira wondituma Ine.


Ngati wina wa osakhulupirira akuitanani, ndipo mufuna kupita; mudye chomwe chiikidwa kwa inu, osafunsa kanthu, chifukwa cha chikumbumtima.


Chomwechonso Ambuye analamulira kuti iwo amene alalikira Uthenga Wabwino akhale ndi moyo ndi Uthenga Wabwino.