Mateyu 10:40 - Buku Lopatulika40 Iye wakulandira inu, andilandira Ine, ndi wakundilandira Ine, amlandira Iye amene ananditumiza Ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Iye wakulandira inu, andilandira Ine, ndi wakundilandira Ine, amlandira Iye amene ananditumiza Ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 “Munthu wokulandirani inu, amandilandira Ine ndemwe. Ndipo wondilandira Ine, amalandiranso Iye uja amene adandituma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 “Iye amene alandira inu alandira Ine, ndipo amene alandira Ine alandiranso amene anandituma Ine. Onani mutuwo |