Luka 10:10 - Buku Lopatulika10 ndipo salandira inu, m'mene mwatuluka kumakwalala ake nenani, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndipo salandira inu, m'mene mwatuluka kumakwalala ake nenani, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma kumudzi kumene mukaloŵe, anthu nkupanda kukulandirani bwino, mukapite m'miseu yam'mudzimo, nkukanena kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Koma mukalowa mʼmudzi ndipo osalandiridwa bwino, kapiteni ku misewu mʼmudzimo nʼkukanena kuti, Onani mutuwo |