Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Genesis 23:7 - Buku Lopatulika

Ndipo anauka Abrahamu naweramira anthu a m'dzikomo, ana a Hiti.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anauka Abrahamu naweramira anthu a m'dzikomo, ana a Hiti.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Abrahamu adaimirira nkuŵeramira anthuwo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tsono Abrahamu anayimirira naweramira anthu a dziko la Hiti aja

Onani mutuwo



Genesis 23:7
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Kanani anabala Sidoni woyamba wake, ndi Heti,


Ndipo anatukula maso ake, nayang'ana, taonani, anthu atatu anaima pandunji pake; pamene anaona iwo, anawathamangira kuchoka ku khomo la hema kukakomana nao, nawerama pansi, nati,


Ndipo anadza ku Sodomu madzulo amithenga awiri; ndipo Loti anakhala pa chipata cha Sodomu, ndipo Loti anaona iwo, nauka kuti akakomane nao, ndipo anaweramitsa pansi nkhope yake.


Ndipo Abrahamu anawerama pamaso pa anthu a m'dzikomo.


Mutimvere ife mfumu, ndinu kalonga wamkulu pakati pa ife; muike wakufa wanu m'manda mwathu mosankhika: palibe munthu yense wa ife adzakaniza manda ake, kuti muike wakufa wanu.


Ndipo ananena nao, kuti, Ngati mukandivomereza kuti ndiike wakufa wanga ndisamthirenso maso, mundimvere ine, mundinenere ine kwa Efuroni mwana wake wa Zohari,


Ndipo Yosefe anatulutsa iwo pakati pa maondo ake, nawerama ndi nkhope yake pansi.


Woyanjana ndi ambiri angodziononga; koma lilipo bwenzi lipambana ndi mbale kuumirira.


Londolani mtendere ndi anthu onse, ndi chiyeretso chimene, akapanda ichi, palibe mmodzi adzaona Ambuye:


Chotsalira, khalani nonse a mtima umodzi, ochitirana chifundo, okondana ndi abale, achisoni, odzichepetsa;