Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 40:21 - Buku Lopatulika

nalowa nalo likasa mu chihema, napachika nsalu yotchinga, natchinga likasa la mboni; monga Yehova adamuuza Mose.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nalowa nalo likasa m'Kachisi, napachika nsalu yotchinga, natchinga likasa la mboni; monga Yehova adamuuza Mose.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kenaka adaika bokosilo m'malo opatulika, ndipo adaika nsalu zochingira. Motero adachinga bokosi laumboni, monga momwe Chauta adamlamulira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka analowetsa bokosilo mʼchihema ndipo anapachika katani ndi kubisa bokosi la umboni monga momwe Yehova analamulira iye.

Onani mutuwo



Eksodo 40:21
5 Mawu Ofanana  

Ndipo uzitchinga nsalu yotchinga pa zokowerazo, nulowetse likasa la mboni kukati kwa nsalu yotchinga; ndipo nsalu yotchingayo idzakugawirani pakati pa malo opatulika ndi malo opatulika kwambiri.


likasa, ndi mphiko zake, chotetezerapo, ndi nsalu yotchinga yotseka;


Ndipo ukaikemo likasa la mboni, nutchinge likasalo ndi nsalu yotchingayo.


ndipo wansembeyo aviike chala chake m'mwazimo, nawaze mwaziwo kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova chakuno cha nsalu yotchinga, ya malo opatulika.