Levitiko 4:6 - Buku Lopatulika6 ndipo wansembeyo aviike chala chake m'mwazimo, nawaze mwaziwo kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova chakuno cha nsalu yotchinga, ya malo opatulika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndipo wansembeyo aviike chala chake m'mwazimo, nawaze mwaziwo kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova chakuno cha nsalu yotchinga, ya malo opatulika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Apo aviike chala chake m'magazi, ndi kuwaza magaziwo kasanu ndi kaŵiri patsogolo pa nsalu yochinga malo oyera pamaso pa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iye aviyike chala chake mʼmagazi, ndipo awawaze kasanu ndi kawiri pamaso pa Yehova, patsogolo pa katani yotchinga malo wopatulika. Onani mutuwo |