Eksodo 40:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo anaika gomelo m'chihema chokomanako, pa mbali ya kumpoto ya Kachisi, kunja kwa nsalu yotchinga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo anaika gomelo m'chihema chokomanako, pa mbali ya kumpoto ya Kachisi, kunja kwa nsalu yotchinga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono m'chihema chamsonkhanomo adaikamo tebulo, chakumpoto kwa malo opatulika, kunja kwa nsalu yochinga ija, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mose anayika tebulo mu tenti ya msonkhano kumpoto kwa chihema, kunja kwa katani, Onani mutuwo |