Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 25:7 - Buku Lopatulika

miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ulandirenso miyala yokoma ya onikisi, ndiponso miyala ina yoti uike pa chovala chaunsembe cha efodi, ndi pa chovala chapachifuwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

miyala yokongola ya mtundu wa onikisi ndi ina yabwino yoyika pa efodi ndi pa chovala cha pachifuwa.

Onani mutuwo



Eksodo 25:7
6 Mawu Ofanana  

golide wa dziko ali wabwino; ndimonso muli bedola ndi mwala wasohamu.


Ndipo zovala azisoka ndi izi: chapachifuwa ndi efodi, ndi mwinjiro, ndi malaya opikapika, ndi nduwira, ndi mpango; tero apangire Aroni mbale wako ndi ana ake zovala zopatulika, kuti andichitire Ine ntchito ya nsembe.


Ndi akulu anabwera nayo miyala yasohamu, ndi miyala yoti aiike kuefodi, ndi kuchapachifuwa;


ndi miyala yasohamu, ndi miyala yoika ya efodi, ndi ya chapachifuwa.


Ana a maso ake akunga nkhunda pambali pa mitsinje ya madzi; otsukidwa ndi mkaka, okhala pa mitsinje yodzala.