Eksodo 35:27 - Buku Lopatulika27 Ndi akulu anabwera nayo miyala yasohamu, ndi miyala yoti aiike kuefodi, ndi kuchapachifuwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndi akulu anabwera nayo miyala yasohamu, ndi miyala yoti aiike kuefodi, ndi kuchapachifuwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Ndipo atsogoleri adabwera ndi miyala ya onikisi ndi miyala ina yoika pa chovala cha efodi ndiponso pa chovala chapachifuwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Atsogoleri anabweretsa miyala ya onikisi ndi miyala yokongola yoyika pa efodi ndi chovala chapachifuwa. Onani mutuwo |