Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 35:9 - Buku Lopatulika

9 ndi miyala yasohamu, ndi miyala yoika ya efodi, ndi ya chapachifuwa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 ndi miyala yasohamu, ndi miyala yoika ya efodi, ndi ya chapachifuwa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 miyala ya mtundu wa onikisi ndi ina yokoma yoika pa chovala chaunsembe cha efodi ndiponso pa chovala chapachifuwa.’ ”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 miyala yokongola ya mtundu wa onikisi ndi ina yabwino yoyika pa Efodi ndi pa chovala cha pachifuwa.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:9
7 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


miyala yaberulo, ndi miyala yoika paefodi, ndi pachapachifuwa.


Ndipo utenge miyala iwiri yaberulo, nulochepo maina a ana a Israele;


Ndipo abwere yense wa mtima waluso mwa inu, napange zonse zimene Yehova analamula;


ndi mafuta akuunikira, ndi zonunkhira za mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa