Eksodo 35:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo abwere yense wa mtima waluso mwa inu, napange zonse zimene Yehova analamula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo abwere yense wa mtima waluso mwa inu, napange zonse zimene Yehova anauza; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 “Anthu onse aluso pakati panupa abwere, ndipo apange zonse zimene Chauta adalamula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Anthu onse aluso pakati panu abwere ndi kupanga zonse zimene Yehova walamula: Onani mutuwo |