Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 35:8 - Buku Lopatulika

8 ndi mafuta akuunikira, ndi zonunkhira za mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 ndi mafuta akuunikira, ndi zonunkhira za mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 mafuta anyale, zonunkhira zopangira mafuta odzozera, ndiponso zopangira lubani wonunkhira bwino,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 mafuta anyale a olivi, zonunkhiritsa mafuta odzozera ndi zopangira lubani wonunkhira;

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:8
7 Mawu Ofanana  

Ndipo uuze ana a Israele akutengere mafuta a azitona oyera opera akuunikira, kuti awalitse nyali kosalekeza.


Udzitengerenso zonunkhira zomveka, mure woyenda masekeli mazana asanu ndi sinamoni wonunkhira wa limodzi la magawo awiri a mureyo, ndilo masekeli mazana awiri kudza makumi asanu, ndi nzimbe zonunkhira mazana awiri kudza makumi asanu,


ndi guwa la nsembe lofukizapo, ndi guwa la nsembe yopsereza ndi zipangizo zake zonse, ndi mkhate wosambiramo ndi tsinde lake.


ndi zonunkhira, ndi mafuta akuunikira, ndi mafuta odzoza, ndi chofukiza za fungo lokoma.


ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


ndi miyala yasohamu, ndi miyala yoika ya efodi, ndi ya chapachifuwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa