Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 35:7 - Buku Lopatulika

7 ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 chikopa chankhosa chonyika mu utoto wofiira, zikopa zambuzi, matabwa a mtengo wa kasiya,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 zikopa za nkhosa zazimuna za utoto wofiira ndi zikopa za akatumbu; matabwa amtengo wa mkesha,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 35:7
4 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Ndipo uzipangira hema chophimba cha zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi chophimba za zikopa za akatumbu pamwamba pake.


ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi;


ndi mafuta akuunikira, ndi zonunkhira za mafuta odzoza, ndi chofukiza cha fungo lokoma;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa