Eksodo 35:6 - Buku Lopatulika6 ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 ndi lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa, ndi ubweya wa mbuzi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 thonje lobiriŵira, lofiirira ndi lofiira. Azibweranso ndi nsalu yokoma yabafuta, nsalu zopangidwa ndi ubweya wambuzi, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 nsalu zobiriwira, zapepo, zofiira, nsalu zofewa; ubweya wambuzi; Onani mutuwo |