Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Eksodo 21:12 - Buku Lopatulika

Iye amene akantha munthu kotero kuti wafa, aphedwe ndithu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iye amene akantha munthu kotero kuti wafa, aphedwe ndithu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Munthu aliyense amene amenya mnzake namupha, nayenso aphedwe ndithu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Munthu aliyense amene amenya mnzake namupha, iyenso ayenera kuphedwa.

Onani mutuwo



Eksodo 21:12
11 Mawu Ofanana  

Zoonatu mwazi wanu wa miyoyo yanu ndidzafuna; padzanja la zinyama zonse ndidzaufuna: ndi padzanja la munthu, padzanja la mbale wake wa munthu ndidzaufuna moyo wa munthu.


Amene akhetsa mwazi wa munthu, ndi munthunso mwazi wake udzakhetsedwa: chifukwa m'chifanizo cha Mulungu Iye anampanga munthu.


Ndipo Davide anati kwa Natani, Ndinachimwira Yehova. Natani nati kwa Davide, Ndiponso Yehova wachotsa tchimo lanu, simudzafa.


Ndipo akapanda kumchitira izi zitatu, azituluka chabe, osaperekapo ndalama.


Munthu akakantha munthu mnzake aliyense kuti afe, amuphe ndithu.


Pomwepo Yesu ananena kwa iye, Tabweza lupanga lako m'chimakemo, pakuti onse akugwira lupanga adzaonongeka ndi lupanga.


Wotembereredwa iye wakukantha mnansi wake m'tseri. Ndi anthu onse anene, Amen.