Genesis 9:6 - Buku Lopatulika6 Amene akhetsa mwazi wa munthu, ndi munthunso mwazi wake udzakhetsedwa: chifukwa m'chifanizo cha Mulungu Iye anampanga munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Amene akhetsa mwazi wa munthu, ndi munthunso mwazi wake udzakhetsedwa: chifukwa m'chifanizo cha Mulungu Iye anampanga munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Aliyense wopha munthu, nayenso adzaphedwa, pakuti munthu adalengedwa muchifaniziro cha Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “Aliyense wopha munthu, adzaphedwanso ndi munthu; pakuti Mulungu analenga munthu mʼchifanizo chake. Onani mutuwo |