Genesis 9:7 - Buku Lopatulika7 Ndi inu, mubalane, muchuluke; muswane padziko lapansi, nimuchuluke m'menemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi inu, mubalane, muchuluke; muswane pa dziko lapansi, nimuchuluke m'menemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsopano mubalane, kuti zidzukulu zanu zidzachulukane ndi kudzabalalika pa dziko lonse lapansi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Inu muberekane ndi kuchulukana kuti mudzaze dziko lonse lapansi ndi kuligonjetsa.” Onani mutuwo |