Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 9:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Mulungu ananena kwa Nowa ndi kwa ana ake pamodzi naye, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Mulungu ananena kwa Nowa ndi kwa ana ake pamodzi naye, kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Mulungu adauza Nowa ndi ana ake kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Mulungu anawuza Nowa ndi ana ake kuti,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 9:8
3 Mawu Ofanana  

Tsiku lomwelo Yehova anapangana chipangano ndi Abramu, nati, Ndidzapatsa mbeu zako dziko ili, kuyambira pamtsinje wa ku Ejipito kufikira pamtsinje waukulu, mtsinje wa Yufurate:


Ndi inu, mubalane, muchuluke; muswane padziko lapansi, nimuchuluke m'menemo.


Ndipo Ine, taonani, Ine ndikhazikitsa pangano langa pamodzi ndi inu, ndi mbeu zanu pambuyo panu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa