Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Genesis 9:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo Ine, taonani, Ine ndikhazikitsa pangano langa pamodzi ndi inu, ndi mbeu zanu pambuyo panu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo Ine, taonani, Ine ndikhazikitsa pangano langa pamodzi ndi inu, ndi mbeu zanu pambuyo panu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 “Tsopano ndikuchita nanu chipangano, pamodzi ndi zidzukulu zanu,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 “Tsopano Ine ndapangana ndi iwe ndi zidzukulu zako zamʼtsogolomo,

Onani mutuwo Koperani




Genesis 9:9
11 Mawu Ofanana  

kudalitsa ndidzakudalitsa iwe, kuchulukitsa ndidzachulukitsa mbeu zako monga nyenyezi za kumwamba, monga mchenga wa m'mphepete mwa nyanja; ndipo mbeu zako zidzagonjetsa chipata cha adani ao;


Koma ndidzakhazikitsa ndi iwe pangano langa; ndipo udzalowa m'chingalawamo iwe ndi ana ako ndi mkazi wako, ndi akazi a ana ako pamodzi ndi iwe.


ndi zamoyo zonse zili pamodzi ndi inu, zouluka, ng'ombe, ndi zinyama zonse za dziko lapansi, pamodzi ndi inu; zonse zotuluka m'chingalawa, zinyama zonse za dziko lapansi.


Ndipo ndidzakhazikitsa pangano langa pamodzi ndi inu; zamoyo zonse sizidzamalizidwanso konse ndi madzi a chigumula; ndipo sikudzakhalanso konse chigumula cha kuononga dziko lapansi.


Ndipo Mulungu anati kwa Nowa, Ichi ndi chizindikiro cha pangano ndalikhazikitsa popangana ndi Ine ndi zamoyo zonse za padziko lapansi.


Ndipo Mulungu ananena kwa Nowa ndi kwa ana ake pamodzi naye, kuti,


Pakuti Yehova atero: Ngati mukhoza kuswa pangano langa la usana ndi pangano langa la usiku, kuti usakhalenso usana ndi usiku, m'nyengo yao;


wakunena za Mwana wake, amene anabadwa, wa mbeu ya Davide, monga mwa thupi,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa