Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo akapanda kumchitira izi zitatu, azituluka chabe, osaperekapo ndalama.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo akapanda kumchitira izi zitatu, azituluka chabe, osaperekapo ndalama.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Akapanda kumchitira zimenezi, ammasule kuti akhale mfulu, koma osalandirapo ndalama.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Koma ngati sangathe kumuchitira zonsezi, ndiye amuleke apite popanda kulipira kanthu.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:11
2 Mawu Ofanana  

Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.


Iye amene akantha munthu kotero kuti wafa, aphedwe ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa