Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:10 - Buku Lopatulika

10 Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Akakwatira mkazi wina, ayenera kupitirira kumpatsa woyambayo chakudya ndi zovala. Azimlolanso zonse zomuyenera ngati mkazi wake, monga ankachitira kale.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ngati akwatira mkazi wina, asamumane woyambayo chakudya ngakhale chovala ndipo apiritirize kugona naye ngati mkazi wake.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:10
3 Mawu Ofanana  

Ndipo akapanda kumchitira izi zitatu, azituluka chabe, osaperekapo ndalama.


Koma ngati amtomera mwana wake wamwamuna, amchitire monga kuyenera ana aakazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa