Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Eksodo 21:10 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Ngati akwatira mkazi wina, asamumane woyambayo chakudya ngakhale chovala ndipo apiritirize kugona naye ngati mkazi wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

10 Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Akakwatira mkazi wina, ayenera kupitirira kumpatsa woyambayo chakudya ndi zovala. Azimlolanso zonse zomuyenera ngati mkazi wake, monga ankachitira kale.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:10
3 Mawu Ofanana  

Koma ngati sangathe kumuchitira zonsezi, ndiye amuleke apite popanda kulipira kanthu.


Ngati anamusankha kuti akhale mkazi wa mwana wake, ayenera kumusunga ngati mwana wake wamkazi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa