Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:9 - Buku Lopatulika

9 Koma ngati amtomera mwana wake wamwamuna, amchitire monga kuyenera ana aakazi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Koma ngati amtomera mwana wake wamwamuna, amchitire monga kuyenera ana akazi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Akaganiza zopatsa mwana wake mkaziyo, azidzamsunga ngati mwana wake wamkazi ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ngati anamusankha kuti akhale mkazi wa mwana wake, ayenera kumusunga ngati mwana wake wamkazi.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:9
2 Mawu Ofanana  

Akamtengera mkazi wina, asachepetse chakudya chake, zovala zake, ndi za ukwati zakezake.


Akapanda kumkonda mbuye wake, amene anamtoma mwini yekha, azilola kuti amuombole; alibe mphamvu yakumgulitsa kwa anthu achilendo, popeza wachita naye monyenga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa