Mateyu 26:52 - Buku Lopatulika52 Pomwepo Yesu ananena kwa iye, Tabweza lupanga lako m'chimakemo, pakuti onse akugwira lupanga adzaonongeka ndi lupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201452 Pomwepo Yesu ananena kwa iye, Tabweza lupanga lako m'chimakemo, pakuti onse akugwira lupanga adzaonongeka ndi lupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa52 Apo Yesu adamuuza kuti, “Bwezera lupangalo m'chimake, pakuti onse ogwira lupanga adzaphedwa ndi lupanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero52 Yesu anati kwa iye, “Bwezera lupanga lako mʼchimake, chifukwa onse amene amapha ndi lupanga adzafa ndi lupanga. Onani mutuwo |