2 Samueli 12:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Davide anati kwa Natani, Ndinachimwira Yehova. Natani nati kwa Davide, Ndiponso Yehova wachotsa tchimo lanu, simudzafa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Davide anati kwa Natani, Ndinachimwira Yehova. Natani nati kwa Davide, Ndiponso Yehova wachotsa tchimo lanu, simudzafa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 “Ndidachimwira Chauta.” Natani adati, “Chauta wakukhululukirani machimo anu, simufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kenaka Davide anati kwa Natani, “Ine ndachimwira Yehova.” Natani anayankha kuti, “Yehova wachotsa tchimo lanu. Simufa ayi. Onani mutuwo |