Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 12:12 - Buku Lopatulika

12 Pakuti iwe unachichita m'tseri; koma Ine ndidzachita chinthu ichi pamaso pa Aisraele onse, dzuwa lili nde.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Pakuti iwe unachichita m'tseri; koma Ine ndidzachita chinthu ichi pamaso pa Aisraele onse, dzuwa lili nde.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Iwe unkachita zimenezo m'seri, koma Ine ndidzazichita pamaso pa Aisraele onse, masana ndithu.’ ” Apo Davide adauza Natani kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Iwe unachita zimenezi mwamseri koma Ine ndidzachita izi masanasana Aisraeli onse akuona.’ ”

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 12:12
7 Mawu Ofanana  

Chomwecho iwo anayalira Abisalomu hema pamwamba pa nyumba; ndipo Abisalomu analowa kwa akazi aang'ono a atate wake pamaso pa Aisraele onse.


mkazi wanga aperere wina; wina namuike kumbuyo.


Palibe mdima kapena mthunzi wa imfa, kuti ochita zopanda pake abisaleko.


Pakuti Mulungu adzanena mlandu wa zochita zonse, ndi zobisika zonse, ngakhale zabwino ngakhale zoipa.


Chifukwa chake musaweruze kanthu isanadze nthawi yake, kufikira akadze Ambuye, amenenso adzaonetsera zobisika za mdima, nadzasonyeza zitsimikizo za mtima; ndipo pamenepo yense adzakhala nao uyamiko wake wa kwa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa