2 Samueli 12:14 - Buku Lopatulika14 Koma popeza pakuchita ichi munapatsa chifukwa chachikulu kwa adani a Yehova cha kuchitira mwano, mwanayonso wobadwira inu adzafa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma popeza pakuchita ichi munapatsa chifukwa chachikulu kwa adani a Yehova cha kuchitira mwano, mwanayonso wobadwira inu adzafa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Komabe, popeza kuti pochita zimenezi mwanyoza Chauta kotheratu, mwana amene akubalireniyo adzafa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Komabe, popeza pochita zimenezi mwachititsa kuti adani a Yehova amunyoze, mwana amene akubalireniyo adzafa.” Onani mutuwo |