Eksodo 21:13 - Buku Lopatulika13 Koma akapanda kumlalira, koma Mulungu akalola akomane ndi mnzake, ndidzakuikirani pothawirapo iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma akapanda kumlalira, koma Mulungu akalola akomane ndi mnzake, ndidzakuikirani pothawirapo iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma ikakhala ngozi, kuti sadaganize konse zomupha mnzakeyo, angathe kuthaŵira ku malo amene ndidzakupatsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Koma ngati sanachite dala, ndipo Mulungu analola kuti zichitike, iyeyo athawire ku malo kumene ndidzakupatsani. Onani mutuwo |