Eksodo 21:14 - Buku Lopatulika14 Koma munthu akachita dala pa mnzake, kumupha monyenga; uzimchotsa ku guwa langa la nsembe, kuti afe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Koma munthu akachita dala pa mnzake, kumupha monyenga; uzimchotsa ku guwa langa la nsembe, kuti afe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Koma munthu akapha mnzake mwadala mwa njira yonyenga, aphedwe ndithu ngakhale wathaŵira ku guwa langa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Koma ngati munthu akonza chiwembu ndi kupha mnzake mwadala, ameneyo muchotseni ngakhale ku guwa langa lansembe ndipo aphedwe. Onani mutuwo |