Eksodo 21:15 - Buku Lopatulika15 Munthu wakukantha atate wake, kapena amai wake, aphedwe ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Munthu wakukantha atate wake, kapena amai wake, aphedwe ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Munthu aliyense amene amenya bambo wake kapena mai wake, aphedwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Munthu aliyense amene amenya abambo ake kapena mayi ake ayenera kuphedwa. Onani mutuwo |