Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Danieli 1:21 - Buku Lopatulika

Nakhala moyo Daniele mpaka chaka choyamba cha mfumu Kirusi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nakhala moyo Daniele mpaka chaka choyamba cha mfumu Kirusi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo Danieli anali kumeneko mpaka chaka choyamba cha ufumu wa Koresi.

Onani mutuwo



Danieli 1:21
4 Mawu Ofanana  

Chaka choyamba tsono cha Kirusi mfumu ya ku Persiya, kuti akwaniridwe mau a Yehova m'kamwa mwa Yeremiya, Yehova anautsa mzimu wa Kirusi, kuti abukitse mau mu ufumu wake wonse, nawalembenso, ndi kuti,


Atero Kirusi mfumu ya ku Persiya, Yehova Mulungu Wam'mwamba anandipatsa maufumu onse a padziko lapansi, nandilangiza ndimmangire nyumba mu Yerusalemu, ndiwo mu Yuda.


Chaka chachitatu cha Kirusi mfumu ya Persiya, chinavumbulutsidwa chinthu kwa Daniele, amene anamutcha Belitesazara; ndipo chinthucho nchoona, ndicho nkhondo yaikulu; ndipo anazindikira chinthucho, nadziwa masomphenyawo.


Momwemo Daniele amene anakuzikabe pokhala Dariusi mfumu, ndi pokhala mfumu Kirusi wa ku Persiya.