Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Danieli 1:21 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Ndipo Danieli anali kumeneko mpaka chaka choyamba cha ufumu wa Koresi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

21 Nakhala moyo Daniele mpaka chaka choyamba cha mfumu Kirusi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Nakhala moyo Daniele mpaka chaka choyamba cha mfumu Kirusi.

Onani mutuwo Koperani




Danieli 1:21
4 Mawu Ofanana  

Mʼchaka choyamba cha ufumu wa Koresi mfumu ya Perisiya, pofuna kukwaniritsa zimene anayankhula kudzera mwa Yeremiya, Yehova anayika maganizo mu mtima mwa Koresi mfumu ya Perisiya kuti alengeze mʼdziko lake lonse ndi mawu apakamwa ngakhalenso ochita kulemba.


Iye anati, “Koresi mfumu ya Perisiya ikunena kuti, “ ‘Yehova, Mulungu wakumwamba wandipatsa maufumu onse a dziko lapansi, ndipo wandipatsa udindo woti ndimumangire Nyumba ku Yerusalemu mʼdziko la Yuda.


Chaka chachitatu cha Koresi mfumu ya Aperezi, Danieli amene ankatchedwa Belitesezara analandira mawu a vumbulutso. Uthenga wake unali woona ndipo anawumvetsa movutikira. Uthengawu anawumva kudzera mʼmasomphenya.


Choncho Danieli anapeza ufulu pa nthawi ya ulamuliro wa Dariyo ndi ulamuliro wa Koresi wa ku Perisiya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa