Ezara 1:1 - Buku Lopatulika1 Chaka choyamba tsono cha Kirusi mfumu ya ku Persiya, kuti akwaniridwe mau a Yehova m'kamwa mwa Yeremiya, Yehova anautsa mzimu wa Kirusi, kuti abukitse mau mu ufumu wake wonse, nawalembenso, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chaka choyamba tsono cha Kirusi mfumu ya ku Persiya, kuti akwaniridwe mau a Yehova m'kamwa mwa Yeremiya, Yehova anautsa mzimu wa Kirusi, kuti abukitse mau m'ufumu wake wonse, nawalembenso, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chaka choyamba cha ulamuliro wa Kirusi, mfumu ya ku Persiya, Chauta adachitadi zimene adaanena kudzera mwa Yeremiya. Adaika maganizo mumtima mwa Kirusi, ndipo iye adalengeza m'dziko lake lonse ndi mau apakamwa, mpakanso ochita kulemba. Adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼchaka choyamba cha ufumu wa Koresi mfumu ya Perisiya, pofuna kukwaniritsa zimene anayankhula kudzera mwa Yeremiya, Yehova anayika maganizo mu mtima mwa Koresi mfumu ya Perisiya kuti alengeze mʼdziko lake lonse ndi mawu apakamwa ngakhalenso ochita kulemba. Onani mutuwo |