2 Samueli 16:21 - Buku Lopatulika
Ndipo Ahitofele ananena ndi Abisalomu, Mulowe kwa akazi aang'ono a atate wanu amene iye anawasiya kuti asunge nyumbayo; ndipo Aisraele onse adzamva kuti atate wanu aipidwa nanu; pomwepo manja a onse akukhala nanu adzalimba.
Onani mutuwo
Ndipo Ahitofele ananena ndi Abisalomu, Mulowe kwa akazi aang'ono a atate wanu amene iye anawasiya kuti asunge nyumbayo; ndipo Aisraele onse adzamva kuti atate wanu aipidwa nanu; pomwepo manja a onse akukhala nanu adzalimba.
Onani mutuwo
Ahitofele adauza Abisalomu kuti, “Pitani mukaloŵe kwa azikazi a bambo wanu amene adaŵasiya kuti azisunga mudzi. Aisraele onse akadziŵa kuti bambo wanu akuipidwa nanu, onse amene akukutsataniŵa adzalimba mtima.”
Onani mutuwo
Ahitofele anayankha kuti, “Mugone ndi azikazi a abambo anu amene awasiya kuti asamalire nyumba yaufumu. Aisraeli onse adzamva kuti mwachitira abambo anu chinthu chonyansa kotheratu ndipo anthu onse amene ali ndi iwe adzalimbikitsidwa.”
Onani mutuwo