Levitiko 18:8 - Buku Lopatulika8 Usamavula mkazi wa atate wako; ndiye thupi la atate wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Usamavula mkazi wa atate wako; ndiye thupi la atate wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Usachititse manyazi bambo wako pakugona ndi mkazi wake aliyense. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “ ‘Usagonane ndi mkazi wa abambo ako (osakhala amayi okubala). Ukatero ukuchititsa manyazi abambo ako. Onani mutuwo |