2 Samueli 16:22 - Buku Lopatulika22 Chomwecho iwo anayalira Abisalomu hema pamwamba pa nyumba; ndipo Abisalomu analowa kwa akazi aang'ono a atate wake pamaso pa Aisraele onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Chomwecho iwo anayalira Abisalomu hema pamwamba pa nyumba; ndipo Abisalomu analowa kwa akazi aang'ono a atate wake pamaso pa Aisraele onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Motero adamangira Abisalomu hema pa denga la nyumba ya mfumu. Ndipo Abisalomu adapita kukaloŵa kwa azikazi a bambo wake, Aisraele onse akupenya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Choncho anamangira tenti Abisalomu pa denga la nyumba ndipo iye anagona ndi azikazi a abambo ake Aisraeli onse akuona. Onani mutuwo |