Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 10:15 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene Aaramu anaona kuti Aisraele anawathyola, anasonkhana pamodzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene Aaramu anaona kuti Aisraele anawathyola, anasonkhana pamodzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Asiriya ataona kuti agonjetsedwa ndi Aisraele, adasonkanitsa ankhondo ao onse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aaramu ataona kuti agonjetsedwa ndi Aisraeli, anasonkhananso.

Onani mutuwo



2 Samueli 10:15
11 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene ana a Amoni anaona kuti Aaramu anathawa, iwonso anathawa pamaso pa Abisai, nalowa m'mzindamo. Ndipo Yowabu anabwera kuchokera kwa ana a Amoni, nafika ku Yerusalemu.


Ndipo Hadadezere anatumiza mthenga nakatenga Aaramu a ku tsidya la chimtsinje; iwo nafika ku Helamu, ndi Sobaki kazembe wa khamu la nkhondo la Hadadezere anawatsogolera.


Davide anakanthanso Hadadezere, mwana wa Rehobu, mfumu ya ku Zoba, pomuka iye kukadzitengeranso ufumu wake ku chimtsinje cha Yufurate.


Aphokoseranji amitundu, nalingiriranji anthu zopanda pake?


nazima mphamvu ya moto, napulumuka lupanga lakuthwa, analimbikitsidwa pokhala ofooka, anakula mphamvu kunkhondo, anapirikitsa magulu a nkhondo yachilendo.


Ndipo kunali, pamene Yabini mfumu ya ku Hazori anachimva, anatuma kwa Yobabu mfumu ya ku Madoni, ndi kwa mfumu ya ku Simironi, ndi kwa mfumu ya ku Akisafu,


Ndipo mafumu awa onse anasonkhana, nadza namanga pamodzi ku madzi a Meromu, kumthira Israele nkhondo.