Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yoswa 11:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo kunali, pamene Yabini mfumu ya ku Hazori anachimva, anatuma kwa Yobabu mfumu ya ku Madoni, ndi kwa mfumu ya ku Simironi, ndi kwa mfumu ya ku Akisafu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo kunali, pamene Yabini mfumu ya ku Hazori anachimva, anatuma kwa Yobabu mfumu ya ku Madoni, ndi kwa mfumu ya ku Simironi, ndi kwa mfumu ya ku Akisafu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mbiri ya zimene zinkachitikazi idamfika Yabini, mfumu ya ku Hazori. Motero iyeyo adatumiza uthenga kwa Yobabu mfumu ya ku Madoni, ndiponso kwa mafumu a ku Simironi ndi Akisafu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yabini, mfumu ya Hazori, inamva zimene zinachitikazi. Tsono inatumiza uthenga kwa Yobabu mfumu ya Madoni, ndiponso kwa mafumu a ku Simironi ndi Akisafu.

Onani mutuwo Koperani




Yoswa 11:1
19 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene Aaramu anaona kuti Aisraele anawathyola, anasonkhana pamodzi.


Benabinadabu ku mtunda wa Dori, mkazi wake ndiye Tafati mwana wa Solomoni;


Ndipo chifukwa chake cha msonkho uja anausonkhetsa mfumu Solomoni ndi chimenechi; kuti amange nyumba ya Yehova, ndi nyumba ya iye yekha, ndi Milo, ndi linga la Yerusalemu, ndi Hazori, ndi Megido, ndi Gezere.


Masiku a Peka mfumu ya Israele anadza Tigilati-Pilesere mfumu ya Asiriya, nalanda Iyoni, ndi Abele-Beti-Maaka, ndi Yanowa, ndi Kedesi, ndi Hazori, ndi Giliyadi, ndi Galileya, dziko lonse la Nafutali; nawatenga andende kunka nao ku Asiriya.


Yehova, dzanja lanu litukulidwa, koma iwo saona; koma iwo adzaona changu chanu cha kwa anthu, nadzakhala ndi manyazi; inde moto udzamaliza adani anu.


Pamene udulitsa pamadzi ndili pamodzi ndi iwe; ndi pooloka mitsinje sidzakukokolola; pakupyola pamoto sudzapsa; ngakhale lawi silidzakutentha.


Pamenepo Yoswa ndi Aisraele onse naye, anabwerera kuchigono ku Giligala.


Ndipo Yoswa anabwerera m'mbuyo nthawi imeneyi nalanda Hazori nakantha mfumu yake ndi lupanga; pakuti kale Hazori unali waukulu wa maufumu aja onse.


mfumu ya ku Madoni, imodzi; mfumu ya ku Hazori, imodzi;


mfumu ya ku Simironi-Meroni, imodzi; mfumu ya ku Akisafu, imodzi;


ndi Adama, ndi Rama, ndi Hazori;


anasonkhana kuponyana ndi Yoswa ndi Israele, ndi mtima umodzi.


Koma Sisera anathawira choyenda pansi ku hema wa Yaele mkazi wa Hebere Mkeni; pakuti panali mtendere pakati pa Yabini mfumu ya Hazori, ndi nyumba ya Hebere Mkeni.


Ndipo Yehova anawagulitsa m'dzanja la Yabini mfumu ya Kanani, wochita ufumu ku Hazori; kazembe wake wa nkhondo ndiye Sisera, wokhala ku Haroseti wa amitundu.


Anadza mafumu nathira nkhondo; pamenepo anathira nkhondo mafumu a Kanani. Mu Taanaki, ku madzi a Megido; osatengako phindu la ndalama.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa