Masalimo 2:1 - Buku Lopatulika1 Aphokoseranji amitundu, nalingiriranji anthu zopanda pake? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Aphokoseranji amitundu, nalingiriranji anthu zopanda pake? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Bwanji anthu akunja akufuna kuchita chiwembu? Chifukwa chiyani anthu ameneŵa akulingalira zopandapake? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu? Onani mutuwo |