Masalimo 1:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti Yehova adziwa mayendedwe a olungama; koma mayendedwe a oipa adzatayika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti Yehova adziwa mayendedwe a olungama; koma mayendedwe a oipa adzatayika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Paja Chauta amaŵasamalira anthu ake, koma anthu ochimwa adzaonongeka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama, koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka. Onani mutuwo |