Masalimo 1:5 - Buku Lopatulika5 Chifukwa chake oipa sadzaimirira pa mlanduwo, kapena ochimwa mu msonkhano wa olungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Chifukwa chake oipa sadzaimirira pa mlanduwo, kapena ochimwa mu msonkhano wa olungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nchifukwa chake anthu ochimwa, Mulungu adzaŵazenga mlandu, adzaŵachotsa iwo pakati pa anthu ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo, kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama. Onani mutuwo |