Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 1:14 - Buku Lopatulika

Ndipo Eli anati kwa iye, Udzaleka liti kuledzera? Chotsa vinyo wako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Eli anati kwa iye, Udzaleka liti kuledzera? Chotsa vinyo wako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono adamufunsa kuti, “Mai, kodi mukhala chiledzerere mpaka liti? Pitani, akayambe watha vinyo mwamwayu.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anamufunsa Hana kuti, “Kodi mukhala chiledzerere mpaka liti? Pitani, ayambe wakuchokani vinyo mwamwayo.”

Onani mutuwo



1 Samueli 1:14
12 Mawu Ofanana  

Mukakhala mphulupulu m'dzanja lako, uichotseretu kutali, ndi chisalungamo chisakhale m'mahema mwako.


Ukabweranso kwa Wamphamvuyonse, udzamanga bwino; ukachotsera chosalungama kutali kwa mahema ako.


Udzanena izi kufikira liti? Ndipo mau a pakamwa pako adzakhala ngati namondwe kufikira liti?


Mudzamvumvulukira munthu mpaka liti, kumupha iye, nonsenu, monga khoma lopendekeka, ndi mpanda woweyeseka?


Tasiya m'kamwa mokhota, uike patali milomo yopotoka.


Udzagona mpaka liti, waulesi iwe? Udzauka kutulo tako liti?


Koma ena anawaseka, nanena kuti, Akhuta vinyo walero.


Ndipo anadzazidwa onse ndi Mzimu Woyera, nayamba kulankhula ndi malilime ena, monga Mzimu anawalankhulitsa.


Mwa ichi, mutataya zonama, lankhulani zoona yense ndi mnzake; pakuti tili ziwalo wina ndi mnzake.


Chiwawo chonse, ndi kupsa mtima, ndi mkwiyo, ndi chiwawa, ndi mwano zichotsedwe kwa inu, ndiponso choipa chonse.