Yobu 8:2 - Buku Lopatulika2 Udzanena izi kufikira liti? Ndipo mau a pakamwa pako adzakhala ngati namondwe kufikira liti? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Udzanena izi kufikira liti? Ndipo mau a pakamwa pako adzakhala ngati namondwe kufikira liti? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Kodi udzakhala ukulankhulabe zoterezi mpaka liti? Mau akoŵa akungopita ngati mphepo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Kodi udzakhala ukuyankhula zoterezi mpaka liti? Mawu ako ali ngati mphepo yamkuntho. Onani mutuwo |