Masalimo 62:3 - Buku Lopatulika3 Mudzamvumvulukira munthu mpaka liti, kumupha iye, nonsenu, monga khoma lopendekeka, ndi mpanda woweyeseka? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mudzamvumvulukira munthu mpaka liti, kumupha iye, nonsenu, monga khoma lopendekeka, ndi mpanda woweyeseka? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Kodi nonsenu mudzaukira munthu mpaka liti, kuti mumgwetse pansi ngati khoma lopendekeka, ngati mpanda wogwedezeka? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kodi nonsenu mudzalimbana naye munthu mpaka liti? Kodi mudzamugwetsa pansi ngati khoma losalimba, ngati mpanda wogwedezeka? Onani mutuwo |