Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Machitidwe a Atumwi 2:13 - Buku Lopatulika

13 Koma ena anawaseka, nanena kuti, Akhuta vinyo walero.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Koma ena anawaseka, nanena kuti, Akhuta vinyo walero.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Koma ena ankangoseka nkumati, “Aledzera vinyo watsopano.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Koma ena anawaseka nati, “Aledzera vinyo watsopano.”

Onani mutuwo Koperani




Machitidwe a Atumwi 2:13
10 Mawu Ofanana  

Taonani, m'chifuwa mwanga muli ngati vinyo wosowa popungulira, ngati matumba atsopano akuti aphulike.


M'kamwa mwako munge ngati vinyo woposa, womeza tseketseke bwenzi langa, wolankhulitsa milomo ya ogona tulo.


Ndipo m'phiri limeneli Yehova wa makamu adzakonzera anthu ake onse phwando la zinthu zonona, phwando la vinyo wa pamitsokwe, la zinthu zonona za mafuta okhaokha, la vinyo wansenga wokuntha bwino.


Ndipo iwo a ku Efuremu adzakhala ngati ngwazi, ndi mtima wao udzakondwera ngati ndi vinyo; ndipo ana ao adzachiona nadzakondwera; mtima wao udzakondwerera mwa Yehova.


Yehova wa makamu adzawatchinjiriza; ndipo adzadza, nadzapondereza miyala yoponyera; ndipo adzamva, nadzachita phokoso ngati avinyo; ndipo adzadzazidwa ngati mbale, ngati ngodya za guwa la nsembe.


Pakuti ukoma wake ndi waukulu ndithu, ndi kukongola kwake nkwakukulu ndithu! Tirigu adzakometsera anyamata, ndi vinyo watsopano anamwali.


Pakuti awa sanaledzere monga muyesa inu; pakuti ndi ora lachitatu lokha la tsiku;


Chifukwa chake, ngati Mpingo wonse akasonkhane pamodzi, ndi onse akalankhule malilime, ndipo akalowemo anthu osaphunzira kapena osakhulupirira, kodi sadzanena kuti mwayaluka?


Ndipo musaledzere naye vinyo, m'mene muli chitayiko; komatu mudzale naye Mzimu,


Ndipo Eli anati kwa iye, Udzaleka liti kuledzera? Chotsa vinyo wako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa