Masalimo 92:12 - Buku Lopatulika12 Wolungama adzaphuka ngati mgwalangwa; adzakula ngati mkungudza wa ku Lebanoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Wolungama adzaphuka ngati mgwalangwa; adzakula ngati mkungudza wa ku Lebanoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthu okondweretsa Mulungu zinthu zimaŵayendera bwino ngati mitengo ya mgwalangwa, amakula ngati mikungudza ya ku Lebanoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Anthu olungama adzaphuka ngati mtengo wa mgwalangwa, adzakula ngati mkungudza wa ku Lebanoni; Onani mutuwo |