Masalimo 92:13 - Buku Lopatulika13 Iwo ookedwa m'nyumba ya Yehova, adzaphuka m'mabwalo a Mulungu wathu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Iwo ookedwa m'nyumba ya Yehova, adzaphuka m'mabwalo a Mulungu wathu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ali ngati mitengo yookedwa m'Nyumba ya Chauta, yokondwa m'mabwalo a Nyumba ya Mulungu wathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 odzalidwa mʼnyumba ya Yehova, adzakula bwino mʼmabwalo a Mulungu wathu. Onani mutuwo |